Machitidwe a Atumwi 19:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo pamene ananena izi, anamasula msonkhano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo pamene ananena izi, anamasula msonkhano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Atanena zimenezi, adauza anthu aja kuti azipita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Iye atatha kunena zimenezi anawuza gulu la anthulo kuti libalalike. Onani mutuwo |