Machitidwe a Atumwi 19:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo pamene Paulo anafuna kulowa kwa anthu, ophunzira ake sanamloleze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo pamene Paulo anafuna kulowa kwa anthu, ophunzira ake sanamloleza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Paulo adaafuna kuloŵa pakati pa anthuwo, koma ophunzira sadamloleze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Paulo anafuna kulowa pakati pa gulu la anthu, koma ophunzira anamuletsa. Onani mutuwo |