Machitidwe a Atumwi 19:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo pamene anamva, anadzala ndi mkwiyo, nafuula, nati, Wamkulu ndi Aritemi wa ku Efeso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo pamene anamva, anadzala ndi mkwiyo, nafuula, nati, Wamkulu ndi Aritemi wa ku Efeso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Anthu aja atamva mau ameneŵa, adakwiya kwabasi, nayamba kufuula kuti, “Ndi wamkulu Aritemi wa Aefeso!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Atamva zimenezi, anakwiya kwambiri ndipo anayamba kufuwula kuti, “Wamkulu ndi Atemi.” Onani mutuwo |