Machitidwe a Atumwi 19:23 - Buku Lopatulika23 Nthawi yomweyo kunali phokoso lambiri kunena za Njirayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Nthawi yomweyo kunali phokoso lambiri kunena za Njirayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Nthaŵi yomweyo padabuka chipolowe chachikulu chifukwa cha Njira ya Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Pa nthawi yomweyo panachitika chipolowe chachikulu chifukwa cha Njira ya Ambuye. Onani mutuwo |