Machitidwe a Atumwi 19:22 - Buku Lopatulika22 Pamene anatuma ku Masedoniya awiri a iwo anamtumikira, Timoteo ndi Erasto, iye mwini anakhalabe nthawi mu Asiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pamene anatuma ku Masedoniya awiri a iwo anamtumikira, Timoteo ndi Erasto, iye mwini anakhalabe nthawi m'Asiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono adatuma Timoteo ndi Erasito ku Masedoniya. Ameneŵa anali aŵiri mwa anthu omuthandiza. Koma mwiniwakeyo adakhalirabe ku Asiya kanthaŵi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Iye anatuma anthu awiri amene amamuthandiza, Timoteyo ndi Erasto ku Makedoniya, pamene iye anakhalabe ku Asiya kwa kanthawi. Onani mutuwo |