Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 19:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo panali ana aamuna asanu ndi awiri a Skeva, Myuda, mkulu wa ansembe amene anachita ichi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo panali ana amuna asanu ndi awiri a Skeva, Myuda, mkulu wa ansembe amene anachita ichi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Amene ankachita zimenezi ndi ana aamuna asanu ndi aŵiri a Skeva, mkulu wa ansembe onse wachiyuda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Amene ankachita zimenezi anali ana asanu ndi awiri a Skeva, mkulu wa ansembe wa Chiyuda.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 19:14
2 Mawu Ofanana  

Koma Ayuda enanso oyendayenda, otulutsa ziwanda, anadziyesa kutchula pa iwo amene anali ndi ziwanda dzina la Ambuye Yesu, kuti, Ndikulumbirirani pa Yesu amene amlalika Paulo.


Ndipo unayankha mzimu woipa, nuti kwa iwo, Yesu ndimzindikira, ndi Paulo ndimdziwa, koma inu ndinu ayani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa