Machitidwe a Atumwi 19:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Mulungu anachita zamphamvu za pazokha ndi manja a Paulo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Mulungu anachita zamphamvu za pa zokha ndi manja a Paulo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mulungu adachita zozizwitsa kwambiri kudzera kwa Paulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mulungu anachita zodabwitsa zapadera kudzera mwa Paulo. Onani mutuwo |