Machitidwe a Atumwi 19:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anachita chomwecho zaka ziwiri; kotero kuti onse akukhala mu Asiya anamva mau a Ambuye, Ayuda ndi Agriki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anachita chomwecho zaka ziwiri; kotero kuti onse akukhala m'Asiya anamva mau a Ambuye, Ayuda ndi Agriki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adachita zimenezi pa zaka ziŵiri, kotero kuti anthu onse okhala ku Asiya, Ayuda ndi Agriki omwe, adamva mau a Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Izi zinachitika kwa zaka ziwiri, kotero kuti Ayuda onse ndi Agriki amene amakhala ku Asiya anamva Mawu a Ambuye. Onani mutuwo |