Machitidwe a Atumwi 19:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo panali, pamene Apolo anali ku Korinto, Paulo anapita pa maiko a pamtunda, nafika ku Efeso, napeza ophunzira ena; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo panali, pamene Apolo anali ku Korinto, Paulo anapita pa maiko a pamtunda, nafika ku Efeso, napeza ophunzira ena; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Apolo anali ku Korinto, Paulo adayendera maiko apamtunda, nakafika ku Efeso. Kumeneko adapezako ophunzira ena, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Apolo ali ku Korinto, Paulo anadutsa mʼmayiko a ku mtunda ndipo anafika ku Efeso. Kumeneko anapeza ophunzira ena. Onani mutuwo |