Machitidwe a Atumwi 18:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anachoka kumeneko, nalowa m'nyumba ya munthu, dzina lake Tito Yusto, amene anapembedza Mulungu, nyumba yake inayandikizana ndi sunagoge. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anachoka kumeneko, nalowa m'nyumba ya munthu, dzina lake Tito Yusto, amene anapembedza Mulungu, nyumba yake inayandikizana ndi sunagoge. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Motero adachoka kumeneko napita ku nyumba ya munthu wina, dzina lake Tito Yusto. Iyeyu anali munthu wopembedza Mulungu, ndipo nyumba yake idaayandikana ndi nyumba yamapemphero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo Paulo anatuluka mʼsunagoge napita ku nyumba yoyandikana ndi sunagoge ya Tito Yusto, munthu wopembedza Mulungu. Onani mutuwo |