Machitidwe a Atumwi 18:23 - Buku Lopatulika23 Atakhala kumeneko nthawi, anachoka, napita ku madera osiyanasiyana a dziko la Galatiya ndi la Frijiya, nakhazikitsa ophunzira onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Atakhala kumeneko nthawi, anachoka, napita ku madera osiyanasiyana a dziko la Galatiya ndi la Frijiya, nakhazikitsa ophunzira onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Atakhala kumeneko kanthaŵi ndithu, adachokako nakayendera dziko la Galatiya ndi la Frijiya, akulimbikitsa ophunzira onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Atakhala kwa kanthawi ku Antiokeya, Paulo anachokako nayendera madera onse a ku Galatiya ndi ku Frugiya kulimbikitsa ophunzira onse. Onani mutuwo |