Machitidwe a Atumwi 18:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo pamene anakocheza pa Kesareya, anakwera naulonjera Mpingo, natsikira ku Antiokeya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo pamene anakocheza pa Kesareya, anakwera naulonjera Mpingo, natsikira ku Antiokeya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Pamene adafika ku Kesareya, adapita ku Yerusalemu kukacheza pang'ono ndi mpingo. Kuchokera kumeneko adapita ku Antiokeya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pamene Paulo anafika ku Kaisareya, anakwera kukapereka moni ku mpingo kenaka anatsikira ku Antiokeya. Onani mutuwo |