Machitidwe a Atumwi 18:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo iwo anafika ku Efeso, ndipo iye analekana nao pamenepo: koma iye yekha analowa m'sunagoge, natsutsana ndi Ayuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo iwo anafika ku Efeso, ndipo iye analekana nao pamenepo: koma iye yekha analowa m'sunagoge, natsutsana ndi Ayuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iwo adakafika ku Efeso, ndipo kumeneko Paulo adasiyako Akwila ndi Prisila. Koma iye yekha adaloŵa m'nyumba yamapemphero nakambirana ndi Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Iwo anafika ku Efeso, kumene Paulo anasiyako Prisila ndi Akula. Iye yekha analowa mʼsunagoge nakambirana ndi Ayuda. Onani mutuwo |