Machitidwe a Atumwi 18:13 - Buku Lopatulika13 kuti, Uyu akopa anthu apembedze Mulungu pokana chilamulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 kuti, Uyu akopa anthu apembedze Mulungu pokana chilamulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Iwo adati, “Munthu uyu akukopa anthu kuti azipembedza Mulungu mwa njira zotsutsana ndi Malamulo athu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iwo anati, “Munthu uyu akukopa anthu kuti azipembedza Mulungu mwanjira zotsutsana ndi malamulo athu.” Onani mutuwo |