Machitidwe a Atumwi 18:12 - Buku Lopatulika12 Tsono pamene Galio anali chiwanga cha Akaya, Ayuda ndi mtima umodzi anamuukira Paulo, nanka naye kumpando wachiweruziro, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Tsono pamene Galio anali chiwanga cha Akaya, Ayuda ndi mtima umodzi anamuukira Paulo, nanka naye kumpando wachiweruziro, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pamene Galio anali bwanamkubwa wa ku Akaiya, Ayuda onse pamodzi adaukira Paulo, namtengera ku bwalo la milandu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Galiyo ali mkulu wa boma wa ku Akaya, Ayuda mogwirizana anamugwira Paulo napita naye ku bwalo la milandu. Onani mutuwo |