Machitidwe a Atumwi 18:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anakhala komwe chaka chimodzi kudza miyezi isanu ndi umodzi; naphunzitsa mau a Mulungu mwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anakhala komwe chaka chimodzi kudza miyezi isanu ndi umodzi; naphunzitsa mau a Mulungu mwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Choncho Paulo adakhala komweko chaka chimodzi ndi miyezi isanu ndi umodzi, akuŵaphunzitsa mau a Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Choncho Paulo anakhala kumeneko chaka ndi miyezi isanu ndi umodzi akuphunzitsa Mawu a Mulungu. Onani mutuwo |