Machitidwe a Atumwi 18:10 - Buku Lopatulika10 chifukwa Ine ndili pamodzi ndi iwe, ndipo palibe munthu adzautsana ndi iwe kuti akuipse; chifukwa ndili nao anthu ambiri m'mzinda muno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 chifukwa Ine ndili pamodzi ndi iwe, ndipo palibe munthu adzautsana ndi iwe kuti akuipse; chifukwa ndili nao anthu ambiri m'mudzi muno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 pakuti Ine ndili nawe pamodzi. Palibe munthu adzakukhudza kuti akuchite choipa, ndipo ndili nawo anthu ambiri mumzinda muno.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti Ine ndili nawe, palibe aliyense amene adzakukhudza ndi kukuchitira choyipa, chifukwa mu mzinda muno ndili ndi anthu ambiri.” Onani mutuwo |