Machitidwe a Atumwi 17:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo pamene anamva za kuuka kwa akufa ena anaseka pwepwete; koma ena anati, Tidzakumvanso za chimenechi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo pamene anamva za kuuka kwa akufa ena anaseka pwepwete; koma ena anati, Tidzakumvanso za chimenechi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Pamene anthuwo adamva za kuuka kwa akufa, ena adangoseka. Koma ena adati, “Bwanji mudzatiwuzenso zimenezi tsiku lina.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Atamva za kuuka kwa akufa, ena a iwo anaseka, koma enanso anati, “Ife tikufuna tidzamvenso zimenezi tsiku lina.” Onani mutuwo |