Machitidwe a Atumwi 17:30 - Buku Lopatulika30 Nthawi za kusadziwako tsono Mulungu analekerera; koma tsopanotu alinkulamulira anthu onse ponseponse atembenuke mtima; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Nthawi za kusadziwako tsono Mulungu analekerera; koma tsopanotu alinkulamulira anthu onse ponseponse atembenuke mtima; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Mulungu adaaŵalekerera anthu pa nthaŵi imene iwo anali osadziŵa, koma tsopano akuŵalamula anthu onse ponseponse kuti atembenuke mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Nthawi imene anthu sankadziwa, Mulungu anawalekerera koma tsopano akulamulira kuti anthu onse, kulikonse atembenuke mtima. Onani mutuwo |