Machitidwe a Atumwi 17:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo anaimirira Paulo pakati pa Areopagi nati, Amuna inu a Atene, m'zinthu zonse ndiona kuti muli akupembedzetsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo anaimirira Paulo pakati pa Areopagi nati, Amuna inu a Atene, m'zinthu zonse ndiona kuti muli akupembedzetsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Paulo adaimirira pakati pa bwalo lija la Aeropagi nati, “Inu anthu a ku Atene, pa zonse ndikuwona kuti ndinu anthu opembedza kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Paulo anayimirira mʼbwalo la Areopagi nati: “Inu anthu a ku Atene! Ine ndikuona kuti mʼnjira zonse ndinu opembedza kwambiri. Onani mutuwo |