Machitidwe a Atumwi 17:21 - Buku Lopatulika21 (Koma Aatene onse ndi alendo akukhalamo anakhalitsa nthawi zao, osachita kanthu kena koma kunena kapena kumva cha tsopano.) Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 (Koma Aatene onse ndi alendo akukhalamo anakhalitsa nthawi zao, osachita kanthu kena koma kunena kapena kumva cha tsopano.) Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndiye kuti nzika za ku Atene ndi alendo okhala kumeneko, inali ngati ntchito nthaŵi zonse kumangomvera zatsopano ndi kumazifotokozera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Atene onse ndi alendo amene amakhala kumeneko samachita kanthu kena koma kufotokoza ndi kumvera fundo zatsopano. Onani mutuwo |