Machitidwe a Atumwi 17:20 - Buku Lopatulika20 Pakuti ufika nazo kumakutu athu zachilendo: tifuna tsono kudziwa, izi zitani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pakuti ufika nazo kumakutu athu zachilendo: tifuna tsono kudziwa, izi zitani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pakuti zina zimene mukutiwuzazi nzachilendo, ndipo tikufuna kudziŵa kuti zinthuzi nzotani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iwe ukubweretsa zinthu zina zachilendo mʼmakutu mwathu, ndipo ife tikufuna tidziwe tanthauzo lake.” Onani mutuwo |