Machitidwe a Atumwi 17:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anamgwira, nanka naye ku Areopagi, nati, Kodi tingathe kudziwa chiphunzitso ichi chatsopano uchinena iwe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anamgwira, nanka naye ku Areopagi, nati, Kodi tingathe kudziwa chiphunzitso ichi chatsopano uchinena iwe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Tsono adapita naye ku bwalo lamilandu lotchedwa Areopagi, namuuza kuti, “Ife timati mutidziŵitseko zatsopano zimene mukuphunzitsazi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kenaka iwo anamutenga nafika naye ku bwalo la Areopagi kumene anamufunsa kuti, “Kodi tingadziweko chiphunzitso chatsopano chimene ukuchifotokozachi? Onani mutuwo |