Machitidwe a Atumwi 17:14 - Buku Lopatulika14 Pomwepo abale anatulutsa Paulo amuke kufikira kunyanja; koma Silasi ndi Timoteo anakhalabe komweko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pomwepo abale anatulutsa Paulo amuke kufikira kunyanja; koma Silasi ndi Timoteo anakhalabe komweko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Nthaŵi yomweyo abale aja adatuma anthu ena kuti aperekeze Paulo ku nyanja, koma Silasi ndi Timoteo adakhalira komweko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Nthawi yomweyo abale anatumiza Paulo ku nyanja koma Sila ndi Timoteyo anatsalira ku Bereya. Onani mutuwo |