Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 16:8 - Buku Lopatulika

8 ndipo pamene anapita pambali pa Misiya, anatsikira ku Troasi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ndipo pamene anapita pambali pa Misiya, anatsikira ku Troasi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Motero adapitirira Misiya nakafika ku Troasi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo iwo anadutsa Musiya ndipo anapita ku Trowa.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 16:8
6 Mawu Ofanana  

Chotero tinachokera ku Troasi m'ngalawa, m'mene tinalunjikitsa ku Samotrase, ndipo m'mawa mwake ku Neapoli;


pamene anafika kundunji kwa Misiya, anayesa kunka ku Bitiniya; ndipo Mzimu wa Yesu sanawaloleze;


Koma iwowa adatitsogolera, natilinda ku Troasi.


Ndipo tinapita m'ngalawa kuchokera ku Filipi, atapita masiku a mkate wopanda chotupitsa, ndipo popita masiku asanu tinawapeza ku Troasi; pamenepo tinatsotsa masiku asanu ndi awiri.


Koma pamene ndinadza ku Troasi kudzalalikira Uthenga Wabwino wa Khristu, ndipo pamene padanditsegukira kwa ine pakhomo, mwa Ambuye,


Chofunda chija ndinachisiya ku Troasi kwa Karpo, udze nacho pakudza iwe, ndi mabuku, makamaka zikopa zija zolembedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa