Machitidwe a Atumwi 16:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo anapita padziko la Frijiya ndi Galatiya, atawaletsa Mzimu Woyera kuti asalalikire mau mu Asiya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo anapita pa dziko la Frijiya ndi Galatiya, atawaletsa Mzimu Woyera kuti asalalikire mau m'Asiya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Paulo ndi anzake aja adapitirira dera la Frijiya ndi la Galatiya, pakuti Mzimu Woyera adaaŵaletsa kulalika mau a Mulungu ku Asiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Paulo ndi anzake anadutsa mayiko a Frugiya ndi Galatiya, Mzimu Woyera atawaletsa kulalikira Mawu a Mulungu ku Asiya. Onani mutuwo |