Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 16:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo anamuuza iye mau a Ambuye, pamodzi ndi onse a pabanja pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo anamuuza iye mau a Ambuye, pamodzi ndi onse a pabanja pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Kenaka adamlalikira mau a Ambuye iyeyo ndi onse a m'nyumba mwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Kenaka analalikira mawu a Ambuye kwa iyeyo ndi onse amene anali mʼnyumba mwake.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 16:32
10 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena nao, Mukani kudziko lonse lapansi, lalikirani Uthenga Wabwino kwa olengedwa onse.


Ndipo iwo anati, Ukhulupirire Ambuye Yesu, ndipo udzapulumuka, iwe ndi apabanja ako.


Ndipo anawatenga ora lomwelo la usiku, natsuka mikwingwirima yao; nabatizidwa pomwepo, iye ndi a pabanja pake.


Ine ndili wamangawa wa Agriki ndi wa akunja, wa anzeru ndi wa opusa.


Pakuti Uthenga Wabwino sundichititsa manyazi; pakuti uli mphamvu ya Mulungu yakupulumutsa munthu aliyense wakukhulupirira; kuyambira Myuda, ndiponso Mgriki.


Kwa ine wochepa ndi wochepetsa wa onse oyera mtima anandipatsa chisomo ichi ndilalikire kwa amitundu chuma chosalondoleka cha Khristu;


kotero ife poliralira inu, tinavomera mokondwera kupereka kwa inu si Uthenga Wabwino wa Mulungu wokha, komanso moyo wathu, popeza mudakhala okondedwa kwa ife.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa