Machitidwe a Atumwi 16:23 - Buku Lopatulika23 Pamene anawaonetsa mikwingwirima yambiri, anawaika m'ndende, nauza mdindo kuti awasunge bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Pamene anawaonetsa mikwingwirima yambiri, anawaika m'ndende, nauza mdindo kuti awasunge bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ataŵakwapula kwambiri, adaŵaponya m'ndende, nalamula woyang'anira ndendeyo kuti aŵasunge bwino, angathaŵe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Atawakwapula kwambiri anawaponya mʼndende, nalamula woyangʼanira kuti awasunge mosamalitsa. Onani mutuwo |