Machitidwe a Atumwi 16:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo linagumukira iwo khamulo; ndipo oweruza anawang'ambira malaya ao; nalamulira kuti awakwapule. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo linagumukira iwo khamulo; ndipo oweruza anawang'ambira malaya ao; nalamulira kuti awakwapule. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Anthu onse adagudukira Paulo ndi Silasi, ndipo akulu oweruza milandu aja adaŵang'ambira zovala zao, nalamula kuti aŵakwapule. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Gulu la anthu linatsutsana ndi Paulo ndi Sila, ndipo woweruza milandu analamula kuti avulidwe ndi kumenyedwa. Onani mutuwo |