Machitidwe a Atumwi 16:12 - Buku Lopatulika12 pochokera kumeneko tinafika ku Filipi, mzinda wa ku Masedoniya, waukulu wa m'dzikomo, wa midzi ya Roma; ndipo tidagona momwemo masiku ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 pochokera kumeneko tinafika ku Filipi, mudzi wa ku Masedoniya, waukulu wa m'dzikomo, wa milaga ya Roma; ndipo tidagona momwemo masiku ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kuchokera kumeneko tidapita ku Filipi, mzinda wa m'chigawo choyamba cha m'dera lija la Masedoniya, ndiponso boma la Aroma. Tidakhala mu mzinda umenewo masiku angapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kuchokera kumeneko tinapita ku Filipi, boma la Aroma ndiponso mzinda waukulu wa dera la Makedoniya. Tinakhala kumeneko masiku owerengeka. Onani mutuwo |