Machitidwe a Atumwi 15:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Mulungu, amene adziwa mtima, anawachitira umboni; nawapatsa Mzimu Woyera, monga anatipatsa ife; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Mulungu, amene adziwa mtima, anawachitira umboni; nawapatsa Mzimu Woyera, monga anatipatsa ife; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndipo Mulungu amene amadziŵa mitima ya anthu, adaŵachitira umboni pakuŵapatsa Mzimu Woyera, monga adapatsira ifeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mulungu amene amadziwa mtima wa munthu, Iye anaonetsa kuti anawalandira powapatsa Mzimu Woyera, monga momwe anachita kwa ife. Onani mutuwo |