Machitidwe a Atumwi 15:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo anasonkhana atumwi ndi akulu kuti anene za mlanduwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo anasonkhana atumwi ndi akulu kuti anene za mlanduwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono atumwi ndi akulu a mpingo adasonkhana kuti aiwone bwino nkhaniyi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Atumwi ndi akulu ampingo anasonkhana kuti akambirane za nkhaniyi. Onani mutuwo |