Machitidwe a Atumwi 15:40 - Buku Lopatulika40 Koma Paulo anasankha Silasi, namuka, woikizidwa ndi abale ku chisomo cha Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Koma Paulo anasankha Silasi, namuka, woikizidwa ndi abale ku chisomo cha Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Koma Paulo adasankhula Silasi, ndipo abale ataŵapempherera kuti Ambuye aŵadalitse, adanyamuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Paulo anasankha Sila. Abale atawapempherera kwa Ambuye kuti alandire chisomo, ananyamuka. Onani mutuwo |