Machitidwe a Atumwi 15:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo Yudasi ndi Silasi, okhala eni okha aneneri, anasangalatsa abale ndi mau ambiri, nawalimbikitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo Yudasi ndi Silasi, okhala eni okha aneneri, anasangalatsa abale ndi mau ambiri, nawalimbikitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Yudasi ndi Silasi analinso alaliki, ndipo adalimbikitsa abale aja ndi mau ambiri naŵakhazikitsa mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Yudasi ndi Sila amene analinso aneneri, ananena zambiri zowalimbikitsa ndi kuwapatsa mphamvu abalewo. Onani mutuwo |