Machitidwe a Atumwi 15:31 - Buku Lopatulika31 Pamene anawerenga, anakondwera chifukwa cha chisangalatso chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Pamene anawerenga, anakondwera chifukwa cha chisangalatso chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Pamene iwo adaiŵerenga, adakondwa chifukwa cha mau ake oŵalimbikitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Anthuwo anawerenga kalatayo ndipo abalewo anakondwa chifukwa cha mawu ake achirimbikitso. Onani mutuwo |