Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 15:31 - Buku Lopatulika

31 Pamene anawerenga, anakondwera chifukwa cha chisangalatso chake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Pamene anawerenga, anakondwera chifukwa cha chisangalatso chake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Pamene iwo adaiŵerenga, adakondwa chifukwa cha mau ake oŵalimbikitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Anthuwo anawerenga kalatayo ndipo abalewo anakondwa chifukwa cha mawu ake achirimbikitso.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 15:31
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza ena akutsika ku Yudeya, nawaphunzitsa abale, nati, Mukapanda kudulidwa monga mwambo wa Mose, simungathe kupulumuka.


Nanga bwanji tsopano mulikumuyesa Mulungu, kuti muike pa khosi la ophunzira goli, limene sanathe kunyamula kapena makolo athu kapena ife?


Tsono pamene iwo anamuka anatsikira ku Antiokeya; ndipo anasonkhanitsa khamu, napereka kalatayo.


Ndipo Yudasi ndi Silasi, okhala eni okha aneneri, anasangalatsa abale ndi mau ambiri, nawalimbikitsa.


Kotero Mipingoyo inalimbikitsidwa m'chikhulupiriro, nachuluka m'chiwerengo chao tsiku ndi tsiku.


Khristu anatisandutsa mfulu, kuti tikhale mfulu; chifukwa chake chilimikani, musakodwenso ndi goli la ukapolo.


pakuti ife ndife mdulidwe, akutumikira popembedza ndi Mzimu wa Mulungu, nadzitamandira mwa Khristu Yesu, osakhulupirira m'thupi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa