Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 15:30 - Buku Lopatulika

30 Tsono pamene iwo anamuka anatsikira ku Antiokeya; ndipo anasonkhanitsa khamu, napereka kalatayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Tsono pamene iwo anamuka anatsikira ku Antiokeya; ndipo anasonkhanitsa khamu, napereka kalatayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Tsono otumidwa aja adanyamuka nakafika ku Antiokeya. Adasonkhanitsa mpingo wonse napereka kalata ija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Anthu aja anatumidwa ndipo anafika ku Antiokeya, kumene anasonkhanitsa mpingo pamodzi napereka kalatayo.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 15:30
9 Mawu Ofanana  

Pamenepo iwotu, akubalalika chifukwa cha chisautsocho chidadza pa Stefano, anafikira ku Fenisiya, ndi Kipro, ndi Antiokeya, osalankhula mau kwa wina yense koma kwa Ayuda okha.


Koma panali ena mwa iwo, amuna a ku Kipro, ndi Kirene, amenewo, m'mene adafika ku Antiokeya, analankhula ndi Agriki, ndi kulalikira Uthenga Wabwino wa Ambuye Yesu.


Koma masiku awa aneneri anatsika ku Yerusalemu kudza ku Antiokeya.


Pamenepo chinakomera atumwi ndi akulu ndi Mpingo wonse kusankha anthu a m'gulu lao, ndi kuwatumiza ku Antiokeya ndi Paulo ndi Barnabasi; ndiwo Yudasi wotchedwa Barsabasi, ndi Silasi, akulu a mwa abale; ndipo analembera mau natumiza ndi iwo:


Pamene anawerenga, anakondwera chifukwa cha chisangalatso chake.


Pamene anapita kupyola pamizinda, anapereka kwa iwo malamulo awasunge, amene analamulira atumwi ndi akulu a pa Yerusalemu.


Nchiyani tsono? Adzamva ndithu kuti wafika.


iwowo, m'mene anafika ku Kesareya, anapereka kalata kwa kazembe, naperekanso Paulo kwa iye.


Ndipo khumi ndi awiriwo anaitana unyinji wa ophunzira, nati, Sikuyenera kuti ife tisiye kulalikira mau a Mulungu ndi kutumikira podyerapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa