Machitidwe a Atumwi 15:27 - Buku Lopatulika27 Tatumiza tsono Yudasi ndi Silasi, omwenso adzakuuzani ndi mau zinthu zomwezo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Tatumiza tsono Yudasi ndi Silasi, omwenso adzakuuzani ndi mau zinthu zomwezo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Nchifukwa chake tatuma Yudasi ndi Silasi kuti adzakufotokozereni pakamwa zimene talemba m'kalatayi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nʼchifukwa chake, tikutumiza Yudasi ndi Sila kuti adzachitire umboni ndi mawu a pakamwa pawo za zimene ife talemba. Onani mutuwo |