Machitidwe a Atumwi 15:26 - Buku Lopatulika26 anthu amene anapereka moyo wao chifukwa cha dzina la Yesu Khristu Ambuye wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 anthu amene anapereka moyo wao chifukwa cha dzina la Yesu Khristu Ambuye wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Amene adadzipereka kuti atumikire Ambuye athu Yesu Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 anthu amene anapereka moyo wawo chifukwa cha dzina la Ambuye athu Yesu Khristu. Onani mutuwo |