Machitidwe a Atumwi 15:25 - Buku Lopatulika25 chinatikomera ndi mtima umodzi, tisankhe anthu, ndi kuwatumiza kwa inu pamodzi ndi okondedwa anthu Barnabasi ndi Paulo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 chinatikomera ndi mtima umodzi, tisankhe anthu, ndi kuwatumiza kwa inu pamodzi ndi okondedwa anthu Barnabasi ndi Paulo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Tsono titasonkhana, tavomerezana kusankha anthu ndi kuŵatuma kwa inu. Adzabwera pamodzi ndi okondedwa athu Barnabasi ndi Paulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Tsono ife tagwirizana kuti, tisankhe anthu ena ndi kuwatumiza kwa inu pamodzi ndi abale athu okondedwa Paulo ndi Barnaba, Onani mutuwo |