Machitidwe a Atumwi 15:24 - Buku Lopatulika24 Popeza tamva kuti ena amene anatuluka mwa ife anakuvutani ndi mau, nasocheretsa mitima yanu; amenewo sitinawalamulire; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Popeza tamva kuti ena amene anatuluka mwa ife anakuvutani ndi mau, nasocheretsa mitima yanu; amenewo sitinawalamulira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tamva kuti anthu ena ochokera m'gulu lathu akhala akukuvutani ndi kukusokonezani maganizo. Amenewo sitidaŵatume ndife ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ife tamva kuti anthu ena ochokera pakati pathu, amene sitinawatume anakusokonezani maganizo ndi kukuvutitsani ndi zimene amakuwuzani. Onani mutuwo |