Machitidwe a Atumwi 15:23 - Buku Lopatulika23 Atumwi ndi abale aakulu, kwa abale a mwa amitundu a mu Antiokeya, ndi Siriya, ndi Silisiya, tikupatsani moni: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Atumwi ndi abale akulu kwa abale a mwa amitundu a m'Antiokeya, ndi Siriya, ndi Silisiya, tikulankhulani: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 kuti akapereke kalata yonena kuti, “Abale, ife atumwi pamodzi ndi akulu a mpingo tikuti moni inu abale a ku Antiokeya, a ku Siriya, ndi a ku Silisiya, amene simuli Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 kuti akapereke kalata yonena kuti, Kuchokera kwa atumwi ndi akulu ampingo, abale anu, Kwa anthu a mitundu ina okhulupirira a ku Antiokeya, Siriya ndi Kilikiya: Tikupereka moni. Onani mutuwo |