Machitidwe a Atumwi 15:20 - Buku Lopatulika20 koma kuti tilembere kwa iwo, kuti asale zonyansa za mafano, ndi dama, ndi zopotola, ndi mwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 koma kuti tilembere kwa iwo, kuti asale zonyansa za mafano, ndi dama, ndi zopotola, ndi mwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma tiŵalembere kalata kuŵauza kuti asamadye zimene zili zosayera chifukwa zidaperekedwa kwa mafano. Alewe dama, ndipo asamadye nyama zochita kupotola, alewenso magazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma tiwalembere iwo, kuwawuza kuti asadye chakudya choperekedwa kwa mafano, apewenso dama, asadyenso nyama zochita kupotola kapena kudya magazi. Onani mutuwo |