Machitidwe a Atumwi 15:19 - Buku Lopatulika19 Chifukwa chake ine ndiweruza, kuti tisavute a mwa amitundu amene anatembenukira kwa Mulungu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Chifukwa chake ine ndiweruza, kuti tisavute a mwa amitundu amene anatembenukira kwa Mulungu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 “Nchifukwa chake ine ndikuti, tisaŵavute anthu a mitundu ina amene akutembenuka mtima nkumatsata Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “Chifukwa chake, ine ndikuweruza kuti tisamavute anthu a mitundu ina amene atembenuka mtima kutsata Mulungu. Onani mutuwo |