Machitidwe a Atumwi 15:18 - Buku Lopatulika18 ati Ambuye, amene azidziwitsa zinthu zonsezo chiyambire dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 ati Ambuye, amene azidziwitsa zinthu zonsezo chiyambire dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Akutero ndi Chauta amene adaulula zimenezi kuyambira kalekale.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 zinaululidwa kuyambira kalekale.’ Onani mutuwo |
Chilombo chimene unachiona chinaliko, koma kulibe; ndipo chidzatuluka m'chiphompho chakuya, ndi kunka kuchitayiko. Ndipo adzazizwa iwo akukhala padziko amene dzina lao silinalembedwe m'buku la moyo chiyambire makhazikidwe a dziko lapansi, pakuona chilombo, kuti chinaliko, ndipo kulibe, ndipo chidzakhalako.