Machitidwe a Atumwi 15:17 - Buku Lopatulika17 Kuti anthu otsalira afunefune Ambuye, ndi amitundu onse amene dzina langa linatchulidwa pa iwo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kuti anthu otsalira afunefune Ambuye, ndi amitundu onse amene dzina langa linatchulidwa pa iwo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndidzachita choncho kuti anthu ena onse afunefune Ambuye, ndiye kuti, anthu a mitundu yonse amene amadziŵika ndi dzina langa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 kuti anthu otsalawo afunefune Ambuye, ndi anthu onse a mitundu ina amene atchedwa ndi dzina langa, akutero Ambuye, amene amachita zinthu zimenezi Onani mutuwo |