Machitidwe a Atumwi 15:16 - Buku Lopatulika16 Zikatha izo ndidzabwera, ndidzamanganso chihema cha Davide, chimene chinagwa; ndidzamanganso zopasuka zake, ndipo ndidzachiimikanso: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Zikatha izo ndidzabwera, ndidzamanganso chihema cha Davide, chimene chinagwa; ndidzamanganso zopasuka zake, ndipo ndidzachiimikanso: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “ ‘Zitatha zimenezi ndidzabwerera, ndidzamanganso nyumba ya Davide imene idagwa. Ndidzamanganso zopasuka zake, ndi kuikonzanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “ ‘Zitatha izi Ine ndidzabwerera ndipo ndidzamanganso nyumba ya Davide imene inagwa. Ndidzakonzanso malo amene anagumuka, ndi kuyimanganso, Onani mutuwo |