Machitidwe a Atumwi 15:14 - Buku Lopatulika14 Simoni wabwereza kuti poyamba Mulungu anayang'anira amitundu, kuti atenge mwa iwo anthu a dzina lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Simoni wabwereza kuti poyamba Mulungu anayang'anira amitundu, kuti atenge mwa iwo anthu a dzina lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Simoni wafotokoza za m'mene Mulungu pachiyambi pomwe adakumbukira anthu a mitundu ina, pa kupatula ena pakati pao kuti akhale anthu akeake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Simoni watifotokozera mmene Mulungu poyamba paja anaonetsa kukhudzidwa kwake pomwe anatenga anthu a mitundu ina kukhala ake. Onani mutuwo |