Machitidwe a Atumwi 15:10 - Buku Lopatulika10 Nanga bwanji tsopano mulikumuyesa Mulungu, kuti muike pa khosi la ophunzira goli, limene sanathe kunyamula kapena makolo athu kapena ife? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Nanga bwanji tsopano mulikumuyesa Mulungu, kuti muike pa khosi la ophunzira goli, limene sanatha kunyamula kapena makolo athu kapena ife? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono mukumuyeseranji Mulungu pakuika m'khosi mwa ophunzirawo goli limene ngakhale makolo athu kapena ife tomwe tidalephera kulisenza? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Tsopano, chifukwa chiyani mukuyesa Mulungu poyika goli mʼkhosi la ophunzira, limene ngakhale ife kapena makolo athu sangathe kulisenza? Onani mutuwo |