Machitidwe a Atumwi 14:6 - Buku Lopatulika6 iwo anamva, nathawira kumizinda ya Likaoniya, Listara ndi Deribe, ndi dziko lozungulirapo: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 iwo anamva, nathawira kumidzi ya Likaoniya, Listara ndi Deribe, ndi dziko lozungulirapo: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Atumwi aja atamva zimenezi, adathaŵira ku Listara ndi ku Deribe, mizinda ya ku Likaoniya, ndiponso ku dziko lozungulira mizindayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma atazindikira zimenezi, anathawira ku Lusitra ndi Derbe, mizinda ya ku Lukaoniya, ndiponso ku dziko lozungulira mizindayo, Onani mutuwo |