Machitidwe a Atumwi 14:20 - Buku Lopatulika20 Koma pamene anamzinga ophunzirawo, anauka iye, nalowa m'mzinda; m'mawa mwake anatuluka ndi Barnabasi kunka ku Deribe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma pamene anamzinga ophunzirawo, anauka iye, nalowa m'mudzi; m'mawa mwake anatuluka ndi Barnabasi kunka ku Deribe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma ophunzira ena atasonkhana nkumzungulira, iye adauka naloŵanso mumzindamo. M'maŵa mwake iye ndi Barnabasi adapita ku Deribe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma ophunzira atamuzungulira, Pauloyo anayimirira nalowanso mu mzindawo. Mmawa mwake iye ndi Barnaba anachoka ndi kupita ku Derbe. Onani mutuwo |